Masalimo 63:2 - Buku Lopatulika2 Kuti ndione mphamvu yanu ndi ulemerero wanu, monga ndinakuonani m'malo oyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Kuti ndione mphamvu yanu ndi ulemerero wanu, monga ndinakuonani m'malo oyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndikukhumbira kukuwonani m'malo anu oyera ndi kuwona mphamvu zanu ndi ulemerero wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Inu ndinakuonani ku malo anu opatulika ndipo ndinapenya mphamvu zanu ndi ulemerero wanu. Onani mutuwo |