Masalimo 62:1 - Buku Lopatulika1 Moyo wanga ukhalira chete Mulungu yekha; chipulumutso changa chifuma kwa Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Moyo wanga ukhalira chete Mulungu yekha; chipulumutso changa chifuma kwa Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mtima wanga umakhala chete kuyembekezera Mulungu yekha, pakuti chipulumutso changa chimafumira kwa Iye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Moyo wanga umapeza mpumulo mwa Mulungu yekha; chipulumutso changa chimachokera kwa Iye. Onani mutuwo |