Masalimo 59:15 - Buku Lopatulika15 Ayendeyende ndi kufuna chakudya, nachezere osakhuta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ayendeyende ndi kufuna chakudya, nachezere osakhuta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Amanka nafunafuna chakudya ndipo amangofuula akapanda kukhuta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Iwo amayendayenda kufuna chakudya ndipo amawuwa ngati sanakhute. Onani mutuwo |