Masalimo 58:9 - Buku Lopatulika9 Miphika yanu isanagwire moto waminga, adzaiuluza, yaiwisi ndi yoyaka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Miphika yanu isanagwire moto waminga, adzaiuluza, yaiwisi ndi yoyaka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Miphika yanu isanagwire moto wa nkhuni zaminga, zingakhale zaziŵisi kapena zoyaka, Mulungu aziseseretu nkuzichotsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Miphika yanu isanagwire moto waminga ya mkandankhuku, kaya iyo ndi yobiriwira kapena yowuma, oyipa adzachotsedwa. Onani mutuwo |