Masalimo 58:6 - Buku Lopatulika6 Thyolani mano ao m'kamwa mwao, Mulungu, zulani zitsakano za misona ya mkango, Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Thyolani mano ao m'kamwa mwao, Mulungu, zulani zitsakano za misona ya mkango, Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Inu Mulungu, gululani mano a m'kamwa mwao, phwanyani nsagwada za mikangoyi, Inu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Gululani mano mʼkamwa mwawo, Inu Mulungu, Yehova khadzulani mano a mikango! Onani mutuwo |