Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 58:10 - Buku Lopatulika

10 Wolungama adzakondwera pakuona kubwezera chilango, adzasamba mapazi ake m'mwazi wa woipa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Wolungama adzakondwera pakuona kubwezera chilango, adzasamba mapazi ake m'mwazi wa woipa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Munthu wangwiro adzakondwera poona kulipsirako. Adzasamba mapazi ake m'magazi a anthu oipawo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Olungama adzasangalala poona kubwezera chilango, pamene adzasambitsa mapazi awo mʼmagazi a anthu oyipa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 58:10
16 Mawu Ofanana  

Olungama achiona nakondwera; ndi osalakwa awaseka pwepwete,


muja popondera ine padakhatamira ndi mafuta amkaka, ndi thanthwe linanditsanulira mitsinje ya mafuta a azitona!


Oongoka mtima adzachiona nadzasekera; koma chosalungama chonse chitseka pakamwa pake.


Ndipo olungama adzachiona, nadzaopa, nadzamseka, ndi kuti,


Wolungama adzakondwera mwa Yehova, nadzakhulupirira Iye; ndipo oongoka mtima onse adzalemekeza.


kuti uviike phazi lako m'mwazi, kuti malilime a agalu ako alaweko adani ako.


Koma udzapenya ndi maso ako, nudzaona kubwezera chilango oipa.


Monga kavumvulu angopita, momwemo woipa kuli zii; koma olungama ndiwo maziko osatha.


Olungama akapeza bwino, mzinda usekera; nufuula pakuonongeka oipa.


Kondwerani, amitundu inu, ndi anthu ake; adzalipsira mwazi wa atumiki ake, adzabwezera chilango akumuukira, nadzafafanizira zoipa dziko lake, ndi anthu ake.


Ndipo moponderamo mphesa anamuponda kunja kwa mzinda, ndipo mudatuluka mwazi moponderamo mphesa, kufikira zapakamwa za akavalo, kufikira mastadiya chikwi ndi mazana asanu ndi limodzi.


Kondwera pa iye, m'mwamba iwe, ndi oyera mtima, ndi atumwi, ndi aneneri inu; chifukwa Mulungu anauweruzira kuweruzidwa kwanu.


Adani anu onse, Yehova, atayike momwemo. Koma iwo akukonda Inu akhale ngati dzuwa lotuluka mu mphamvu yake. Ndipo dziko linapumula zaka makumi anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa