Masalimo 58:1 - Buku Lopatulika1 Kodi muli chete ndithu poyenera inu kunena zolungama? Muweruza ana anthu molunjika kodi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Kodi muli chete ndithu poyenera inu kunena zolungama? Muweruza ana anthu molunjika kodi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Kodi mumagamuladi molungama, inu akuluakulu oweruza? Kodi mumaweruzadi anthu mwachilungamo? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Kodi inu olamulira mumayankhuladi molungama? Kodi mumaweruza mwachilungamo pakati pa anthu? Onani mutuwo |