Masalimo 56:7 - Buku Lopatulika7 Kodi adzapulumuka ndi zopanda pake? Gwetsani anthu mumkwiyo, Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Kodi adzapulumuka ndi zopanda pake? Gwetsani anthu mumkwiyo, Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Muŵalange chifukwa cha zoipa zao. Inu Mulungu, muŵakwiyire anthuwo ndi kuŵaononga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Musalole konse kuti athawe; mu mkwiyo wanu Mulungu mugwetse mitundu ya anthu. Onani mutuwo |