Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 56:7 - Buku Lopatulika

7 Kodi adzapulumuka ndi zopanda pake? Gwetsani anthu mumkwiyo, Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Kodi adzapulumuka ndi zopanda pake? Gwetsani anthu mumkwiyo, Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Muŵalange chifukwa cha zoipa zao. Inu Mulungu, muŵakwiyire anthuwo ndi kuŵaononga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Musalole konse kuti athawe; mu mkwiyo wanu Mulungu mugwetse mitundu ya anthu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 56:7
14 Mawu Ofanana  

Pomwepo padagwera ochita zopanda pake. Anawalikha, ndipo sadzatha kuukanso.


Woipa aunguza wolungama, nafuna kumupha.


Iwo akutama kulemera kwao; nadzitamandira pa kuchuluka kwa chuma chao;


Imfa iwagwere modzidzimutsa, atsikire kumanda ali amoyo, pakuti m'mokhala mwao muli zoipa pakati pao.


Koma Inu, Mulungu, mudzawatsitsira kudzenje la chionongeko. Anthu okhetsa mwazi ndi achinyengo masiku ao sadzafikira nusu; koma ine ndidzakhulupirira Inu.


Aonongeni, Ambuye, gawani lilime lao, pakuti ndaona chiwawa ndi ndeu m'mzindamo.


osawapatsa chifukwa ine, athamanga nadzikonza. Galamukani kukomana nane, ndipo penyani.


Kulibe munthu ali ndi mphamvu yolamulira mzimu ndi yakutsekereza mzimu; ngakhale mphamvu tsiku la imfa; munkhondo umo mulibe kumasuka; udyo sudzapulumutsa akuzolowerana nao.


Chifukwa inu munati, Ife tapangana pangano ndi imfa, tavomerezana ndi kunsi kwa manda; pakuti mliri wosefukira sudzatifikira ife; pakuti tayesa mabodza pothawirapo pathu, ndi kubisala m'zonyenga;


Tsanulirani ukali wanu pa amitundu osakudziwani Inu, ndi pa mabanja osaitana dzina lanu; pakuti anadya Yakobo, inde, anamudya namutha, napasula mokhalamo mwake.


ndi kudza ndi kuima pamaso panga m'nyumba ino, imene itchedwa dzina langa, ndi kuti, Talanditsidwa; kuti muchite zonyansa izi?


Inu wa maso osalakwa, osapenya choipa, osakhoza kupenyerera chovuta, mupenyereranji iwo akuchita mochenjerera, ndi kukhala chete pamene woipa ammeza munthu wolungama woposa iye mwini;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa