Masalimo 56:6 - Buku Lopatulika6 Amemezana, alalira, atchereza mapazi anga, popeza alindira moyo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Amemezana, alalira, atchereza mapazi anga, popeza alindira moyo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Amasonkhana okhaokha namabisalira, amalonda mayendedwe anga, amafuna kundipha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iwo amakambirana, amandibisalira, amayangʼanitsitsa mayendedwe anga ndipo amakhala ndi chidwi chofuna kuchotsa moyo wanga. Onani mutuwo |