Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 56:12 - Buku Lopatulika

12 Zowindira Inu Mulungu, zili pa ine, ndidzakuchitirani zoyamika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Zowindira Inu Mulungu, zili pa ine, ndidzakuchitirani zoyamika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Ndiyenera kuchita zimene ndidalumbira kwa Inu Mulungu. Ndidzapereka kwa Inu nsembe zothokozera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Ndiyenera kuchita zomwe ndinalumbira kwa Mulungu; ndidzapereka nsembe zanga zachiyamiko kwa inu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 56:12
16 Mawu Ofanana  

Yehova ndi wanga; sindidzaopa; adzandichitanji munthu?


Ndinalumbira, ndipo ndinatsimikiza mtima, kuti ndidzasamalira maweruzo anu olungama.


Kwezekani, Yehova, mu mphamvu yanu; potero tidzaimba ndi kulemekeza chilimbiko chanu.


Pereka kwa Mulungu nsembe yachiyamiko; numchitire Wam'mwambamwamba chowinda chako.


Windani ndipo chitirani Yehova Mulungu wanu zowindazo; onse akumzinga abwere nacho chopereka cha kwa Iye amene ayenera kumuopa.


Tsiku lomwelo udzati, Ndikuyamikani inu Yehova; pakuti ngakhale munandikwiyira, mkwiyo wanu wachoka, ndipo mutonthoza mtima wanga.


nalonjeza chowinda, nati, Yehova wa makamu, mukapenyera ndithu kusauka kwa mdzakazi wanu, ndi kukumbukira ine, ndi kusaiwala mdzakazi wanu, mukapatsa mdzakazi wanu mwana wamwamuna, ine ndidzampereka kwa Yehova masiku onse a moyo wake, ndipo palibe lumo lidzapita pamutu pake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa