Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 56:11 - Buku Lopatulika

11 Pa Mulungu ndakhulupirira, sindidzaopa; munthu adzandichitanji?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Pa Mulungu ndakhulupirira, sindidzaopa; munthu adzandichitanji?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Ndimadalira Mulungu, sindidzachita mantha konse. Kodi munthu angandichite chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 mwa Mulungu ine ndimadalira ndipo sindidzachita mantha. Kodi munthu angandichite chiyani?

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 56:11
4 Mawu Ofanana  

Yehova ndiye kuunika kwanga ndi chipulumutso changa; ndidzaopa yani? Yehova ndiye mphamvu ya moyo wanga; ndidzachita mantha ndi yani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa