Masalimo 55:22 - Buku Lopatulika22 Umsenze Yehova nkhawa zako, ndipo Iye adzakugwiriziza, nthawi zonse sadzalola wolungama agwedezeke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Umsenze Yehova nkhawa zako, ndipo Iye adzakugwiriziza, nthawi zonse sadzalola wolungama agwedezeke. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Tula kwa Chauta nkhaŵa zako, ndipo Iye adzakuchirikiza. Sadzalola konse kuti wolungama wake agwedezeke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Tulani nkhawa zanu kwa Yehova ndipo Iye adzakulimbitsani; Iye sadzalola kuti wolungama agwe. Onani mutuwo |