Masalimo 55:19 - Buku Lopatulika19 Mulungu adzamva, nadzawasautsa, ndiye wokhalabe chiyambire kale lomwe. Popeza iwowa sasinthika konse, ndipo saopa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Mulungu adzamva, nadzawasautsa, ndiye wokhalabe chiyambire kale lomwe. Popeza iwowa sasinthika konse, ndipo saopa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Mulungu, amene akukhala pa mpando waufumu kuyambira kalekale, adzandimenyera nkhondo, adzaŵatsitsa adani anga chifukwa safuna kusintha khalidwe lao loipa, ndipo saopa Iye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Mulungu amene ali pa mpando wake kwamuyaya, adzandimenyera nkhondo; adzawatsitsa adani anga, chifukwa safuna kusintha njira zawo zoyipa ndipo saopa Mulungu. Onani mutuwo |