Masalimo 55:18 - Buku Lopatulika18 Anaombola moyo wanga kunkhondo, ndikhale mumtendere, pakuti ndiwo ambiri okangana nane. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Anaombola moyo wanga kunkhondo yondilaka, ndikhale mumtendere, pakuti ndiwo ambiri okangana nane. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Adzapulumutsa moyo wanga pa nkhondo imene ndikumenya, pakuti anthu ambiri akukangana nane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Iye amandiwombola ine osavulazidwa pa nkhondo imene yafika kulimbana nane, ngakhale kuti ndi ambiri amene akunditsutsa. Onani mutuwo |