Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 55:16 - Buku Lopatulika

16 Koma ine ndidzafuulira kwa Mulungu; ndipo Yehova adzandipulumutsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Koma ine ndidzafuulira kwa Mulungu; ndipo Yehova adzandipulumutsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Koma ine ndikupempha Chauta, ndipo Iye adzandithandiza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Koma ine ndinafuwulira kwa Mulungu, ndipo Yehova anandipulumutsa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 55:16
6 Mawu Ofanana  

M'malo mwa chikondi changa andibwezera udani; koma ine, kupemphera ndiko.


Ndipo undiitane tsiku la chisautso, ndidzakulanditsa, ndipo iwe udzandilemekeza.


Koma ine, kundikomera kuyandikiza kwa Mulungu. Ndimuyesa Ambuye Yehova pothawirapo ine, kuti ndifotokozere ntchito zanu zonse.


Adzandifuulira Ine ndipo ndidzamyankha; kunsautso ndidzakhala naye pamodzi; ndidzamlanditsa, ndi kumchitira ulemu.


Chomwecho iwowa, ndi onse anali nao, anatsikira kumanda ali ndi moyo, ndi dziko linasunama pa iwo, ndipo anaonongeka pakati pa msonkhano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa