Masalimo 55:14 - Buku Lopatulika14 Tinapangirana upo wokoma, tinaperekeza khamu la anthu popita kunyumba ya Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Tinapangirana upo wokoma, tinaperekeza khamu la anthu popita kunyumba ya Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tinkakambirana nkhani zokoma tili aŵiri, tinkapembedza limodzi m'Nyumba ya Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Mnzanga amene nthawi ina tinkasangalala pa chiyanjano chokoma ku nyumba ya Mulungu. Onani mutuwo |