Masalimo 55:13 - Buku Lopatulika13 Koma ameneyo ndiwe, munthu woyenerana nane, tsamwali wanga, wodziwana nane. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma ameneyo ndiwe, munthu woyenerana nane, tsamwali wanga, wodziwana nane. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma iweyo mnzanga, mnzanga woyenda naye, bwenzi langa wozoloŵerana naye, ndi amene ukuchita zimenezi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Koma iweyo mnzanga, mnzanga woyenda naye, bwenzi langa la pondaapanʼpondepo, ndi amene ukuchita zimenezi. Onani mutuwo |