Masalimo 55:11 - Buku Lopatulika11 M'kati mwake muli kusakaza, chiwawa ndi chinyengo sizichoka m'makwalala ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 M'kati mwake muli kusakaza, chiwawa ndi chinyengo sizichoka m'makwalala ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 M'menemo muli chiwonongeko chokhachokha. M'misika yake muli zopanikizana ndi zonyenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mphamvu zowononga zili pa ntchito mu mzinda; kuopseza ndi mabodza sizichoka mʼmisewu yake. Onani mutuwo |