Masalimo 50:22 - Buku Lopatulika22 Dziwitsani ichi inu oiwala Mulungu, kuti ndingakumwetuleni, ndipo mungasowepo mpulumutsi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Dziwitsani ichi inu oiwala Mulungu, kuti ndingakumwetuleni, ndipo mungasowepo mpulumutsi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 “Ganizani bwino izi tsono, inu amene mumaiŵala Mulungu, kuti ndingakukadzuleni, ndipo palibe amene angakupulumutseni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 “Ganizira izi, iwe amene umayiwala Mulungu kuti ndingakukadzule popanda wokupulumutsa: Onani mutuwo |