Masalimo 50:21 - Buku Lopatulika21 Izi unazichita iwe, ndipo ndinakhala chete Ine; unayesa kuti ndifanana nawe, ndidzakudzudzula, ndi kuchilongosola pamaso pako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Izi unazichita iwe, ndipo ndinakhala chete Ine; unayesa kuti ndifanana nawe, ndidzakudzudzula, ndi kuchilongosola pamaso pako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Iwe wachita zinthu zimenezi, ndipo Ine ndakhala ndili chete. Unalikuganiza kuti ndimafanafana nawe. Koma tsopano ndikukudzudzula ndi kukuwonetsa zimene wachita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Wachita zimenezi ndipo Ine ndinali chete; umaganiza kuti ndine wofanana nawe koma ndidzakudzudzula ndipo ndidzakutsutsa pamaso pako. Onani mutuwo |