Masalimo 50:20 - Buku Lopatulika20 Ukhala, nuneneza mbale wako; usinjirira mwana wa mai wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ukhala, nuneneza mbale wako; usinjirira mwana wa mai wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 “Umakhala pansi nkumachitira mbale wako miseche, inde, umasinjirira mbale wako weniweni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Nthawi zonse umayankhula motsutsana ndi mʼbale wako ndipo umasinjirira mwana wa amayi ako enieni. Onani mutuwo |