Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 50:18 - Buku Lopatulika

18 Pakuona mbala, uvomerezana nayo, nuchita nao achigololo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Pakuona mbala, uvomerezana nayo, nuchita nao achigololo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 “Ukaona mbala umasanduka bwenzi lake, ndipo umayenda ndi anthu achigololo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ukaona wakuba umamutsatira, umachita maere ako pamodzi ndi achigololo

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 50:18
14 Mawu Ofanana  

Ndipo Yonadabu ananena naye, Ugone pa kama wako ndi kudzikokomera ulikudwala; ndipo pamene atate wako akadzakuona unene naye, Mulole mlongo wanga Tamara abwere kundipatsa kudya, nakonzere chakudyacho pamaso panga kuti ndichione ndi kuchidya cha m'manja mwake.


amene alungamitsa woipa pa chokometsera mlandu, nachotsera wolungama chilungamo chake!


Munthu akachita chigololo ndi mkazi wa mwini, popeza wachita chigololo ndi mkazi wa mnansi wake, awaphe ndithu, mwamuna ndi mkazi onse awiri.


Manja ao onse awiri agwira choipa kuchichita ndi changu; kalonga apempha, ndi woweruza aweruza chifukwa cha mphotho; ndi wamkuluyo angonena chosakaza moyo wake; ndipo achiluka pamodzi.


ndi kuti, Ife tikadakhala m'masiku a makolo anthu, sitikadakhala oyanjana nao pa mwazi wa aneneri.


amene ngakhale adziwa kuweruza kwake kwa Mulungu, kuti iwo amene achita zotere ayenera imfa, azichita iwo okha, ndiponso avomerezana ndi iwo akuzichita.


Usafulumira kuika manja pa munthu aliyense, kapena usayanjana nazo zoipa za eni; udzisunge wekha woyera mtima.


Ukwati uchitidwe ulemu ndi onse, ndi pogona pakhale posadetsedwa; pakuti adama ndi achigololo adzawaweruza Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa