Masalimo 50:18 - Buku Lopatulika18 Pakuona mbala, uvomerezana nayo, nuchita nao achigololo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pakuona mbala, uvomerezana nayo, nuchita nao achigololo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 “Ukaona mbala umasanduka bwenzi lake, ndipo umayenda ndi anthu achigololo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ukaona wakuba umamutsatira, umachita maere ako pamodzi ndi achigololo Onani mutuwo |