Masalimo 50:14 - Buku Lopatulika14 Pereka kwa Mulungu nsembe yachiyamiko; numchitire Wam'mwambamwamba chowinda chako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pereka kwa Mulungu nsembe yachiyamiko; numchitire Wam'mwambamwamba chowinda chako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Koma perekani nsembe zanu zothokozera kwa Mulungu, ndipo muchite zimene mudalumbira kwa Wopambanazonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Pereka nsembe zachiyamiko kwa Mulungu, kwaniritsa malonjezo ako kwa Wammwambamwamba. Onani mutuwo |