Masalimo 49:20 - Buku Lopatulika20 Munthu waulemu, koma wosadziwitsa, afanana ndi nyama zakuthengo, afanana nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Munthu waulemu, koma wosadziwitsa, afanana ndi nyama za kuthengo, afanana nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ngakhale munthu akhale wolemera chotani, komabe akasoŵa nzeru, adzafa chabe ngati nyama zakuthengo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Munthu amene ali ndi chuma koma wopanda nzeru adzafa ngati nyama yakuthengo. Onani mutuwo |