Masalimo 49:19 - Buku Lopatulika19 Adzamuka kumbadwo wa makolo ake; sadzaona kuunika nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Adzamuka kumbadwo wa makolo ake; sadzaona kuunika nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 adzafabe nkukakumana ndi makolo ake onse kumanda, kumene sadzaona kuŵala mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 iyeyo adzakakhala pamodzi ndi mʼbado wa makolo ake, amene sadzaonanso kuwala. Onani mutuwo |