Masalimo 49:18 - Buku Lopatulika18 Angakhale anadalitsa moyo wake pokhala ndi moyo, ndipo anthu akulemekeza iwe, podzichitira wekha zokoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Angakhale anadalitsa moyo wake pokhala ndi moyo, ndipo anthu akulemekeza iwe, podzichitira wekha zokoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ngakhale pamene munthuyo ali moyo, amadziyesa wodala, ndipo ngakhale atamandidwe pamene zinthu zikumuyendera bwino, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ngakhale pamene munthuyo ali moyo amadziyesa wodala, ndipo ngakhale atamandidwe pamene zinthu zikumuyendera bwino, Onani mutuwo |