Masalimo 46:8 - Buku Lopatulika8 Idzani, penyani ntchito za Yehova, amene achita zopululutsa padziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Idzani, penyani ntchito za Yehova, amene achita zopululutsa pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Bwerani kuti muwone ntchito za Chauta, m'mene amachitira zozizwitsa pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Bwerani kuti mudzaone ntchito za Yehova, chiwonongeko chimene wachibweretsa pa dziko lapansi. Onani mutuwo |