Masalimo 46:7 - Buku Lopatulika7 Yehova wa makamu ali ndi ife; Mulungu wa Yakobo ndiye pamsanje pathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Yehova wa makamu ali ndi ife; Mulungu wa Yakobo ndiye pamsanje pathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Chauta Wamphamvuzonse ali nafe. Mulungu wa Yakobe ndiye kothaŵira kwathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Yehova Wamphamvuzonse ali ndi ife, Mulungu wa Yakobo ndi linga lathu. Onani mutuwo |