Masalimo 46:6 - Buku Lopatulika6 Amitundu anapokosera, maufumu anagwedezeka, ananena mau, dziko lapansi linasungunuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Amitundu anapokosera, maufumu anagwedezeka, ananena mau, dziko lapansi linasungunuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Mitundu ya anthu ikunjenjemera kwambiri, maufumu akugwedezeka, Mulungu akalankhula mau ake, dziko lapansi likusungunuka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mitundu ikupokosera, mafumu akugwa; Iye wakweza mawu ake, dziko lapansi likusungunuka. Onani mutuwo |