Masalimo 46:11 - Buku Lopatulika11 Yehova wa makamu ali ndi ife, Mulungu wa Yakobo ndiye pamsanje pathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Yehova wa makamu ali ndi ife, Mulungu wa Yakobo ndiye pamsanje pathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chauta Wamphamvuzonse ali nafe, Mulungu wa Yakobe ndiye kothaŵira kwathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yehova Wamphamvuzonse ali ndi ife, Mulungu wa Yakobo ndi linga lathu. Onani mutuwo |