Masalimo 45:17 - Buku Lopatulika17 Ndidzawakumbutsa dzina lanu m'mibadwomibadwo; chifukwa chake mitundu ya anthu idzayamika Inu kunthawi za nthawi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndidzawakumbutsa dzina lanu m'mibadwomibadwo; chifukwa chake mitundu ya anthu idzayamika Inu kunthawi za nthawi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ndidzamveketsa mbiri ku mibadwo yonse, nchifukwa chake mitundu ya anthu idzakutamandani mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ndidzabukitsa mbiri yako mʼmibado yonse; choncho mitundu yonse idzakutamanda ku nthawi za nthawi. Onani mutuwo |