Masalimo 45:15 - Buku Lopatulika15 Adzawatsogolera ndi chimwemwe ndi kusekerera, adzalowa m'nyumba ya mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Adzawatsogolera ndi chimwemwe ndi kusekerera, adzalowa m'nyumba ya mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Akuŵaperekeza ndi chimwemwe ndi chisangalalo pokaloŵa m'nyumba ya mfumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Iwo akuwaperekeza ndi chimwemwe ndi chisangalalo; akulowa mʼnyumba yaufumu. Onani mutuwo |