Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 44:26 - Buku Lopatulika

26 Ukani, tithandizeni, tiomboleni mwa chifundo chanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ukani, tithandizeni, tiomboleni mwa chifundo chanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Dzukani, mubwere kudzatithandiza. Tiwomboleni chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Imirirani ndi kutithandiza, tiwomboleni chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 44:26
5 Mawu Ofanana  

Moyo wanga umamatika ndi fumbi; mundipatse moyo monga mwa mau anu.


Ombolani Israele, Mulungu, m'masautso ake onse.


Koma ine, ndidzayenda mu ungwiro wanga; mundiombole, ndipo ndichitireni chifundo.


Gwirani chikopa chotchinjiriza, ukani kundithandiza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa