Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 44:25 - Buku Lopatulika

25 Pakuti moyo wathu waweramira kufumbi, pamimba pathu pakangamira dziko lapansi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Pakuti moyo wathu waweramira kufumbi, pamimba pathu pakangamira dziko lapansi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Ife tagwa pansi m'fumbi, thupi lathu langoti thapsa pa dothi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Tatsitsidwa pansi mpaka pa fumbi; matupi athu amatirira pa dothi.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 44:25
7 Mawu Ofanana  

Mubisiranji nkhope yanu, ndi kundiyesa mdani wanu?


Muimiranji patali, Yehova? Mubisaliranji m'nyengo za nsautso?


Moyo wanga umamatika ndi fumbi; mundipatse moyo monga mwa mau anu.


Wozunzika ine ndi wofuna kufa kuyambira ubwana wanga; posenza zoopsa zanu, ndithedwa nzeru.


Ndidzachiika m'dzanja la iwo amene avutitsa iwe; amene anena kumoyo wako, Gwada pansi kuti ife tipite; ndipo iwe wagonetsa pamsana pako monga pansi, ndi monga khwalala kwa iwo amene apita pamenepo.


Omwe anadya zolongosoka angosiyidwa m'makwalala; omwe analeredwa navekedwa mlangali afungatira madzala.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa