Masalimo 44:22 - Buku Lopatulika22 Koma, chifukwa cha Inu, tiphedwa tsiku lonse; tiyesedwa ngati nkhosa zakuzipha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma, chifukwa cha Inu, tiphedwa tsiku lonse; tiyesedwa ngati nkhosa zakuzipha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Koma chifukwa cha Inu, adani akutipha tsiku lonse, pamaso pao tili ngati nkhosa zimene akukazipha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Komabe chifukwa cha Inu timakumana ndi imfa tsiku lonse, tili ngati nkhosa zoyenera kuti ziphedwe. Onani mutuwo |