Masalimo 44:21 - Buku Lopatulika21 Mulungu sakadasanthula ichi kodi? Pakuti adziwa zinsinsi za mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Mulungu sakadasanthula ichi kodi? Pakuti adziwa zinsinsi za mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 kodi Mulungu sakadazipeza zimenezi? Paja Iye amadziŵa zinsinsi zonse zamumtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 kodi Mulungu wathu sakanazidziwa zimenezi, pakuti Iye amadziwa zinsinsi zamumtima? Onani mutuwo |