Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 44:19 - Buku Lopatulika

19 mungakhale munatithyola mokhala zilombo, ndi kutiphimba nao mthunzi wa imfa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 mungakhale munatithyola mokhala zilombo, ndi kutiphimba nao mthunzi wa imfa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Komabe Inuyo mwatitswanya ndi kutisiya pakati pa nkhandwe ku chipululu, kumene kuli mdima wandiweyani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Koma Inu mwatiphwanya ndi kuchititsa kuti tikhale ozunzidwa ndi ankhandwe ndipo mwatiphimba ndi mdima waukulu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 44:19
19 Mawu Ofanana  

Phazi langa lagwiratu moponda Iye, ndasunga njira yake, wosapatukamo.


Mdima ndi mthunzi wa imfa ziliyese laolao; mtambo ulikhalire; zonse zodetsa usana bii ziliopse.


Ndili mbale wao wa ankhandwe, ndi mnansi wao wa nthiwatiwa.


Inde, ndingakhale ndiyenda m'chigwa cha mthunzi wa imfa, sindidzaopa choipa; pakuti Inu muli ndi ine; chibonga chanu ndi ndodo yanu, izi zindisangalatsa ine.


Ndafooka ine, ndipo ndachinjizidwa, ndabangula chifukwa cha kumyuka mtima wanga.


Mundimvetse chimwemwe ndi kusekera, kuti mafupawo munawathyola akondwere.


Tsiku limenelo Yehova ndi lupanga lake lolimba ndi lalikulu ndi lamphamvu adzalanga Leviyatani njoka yothamanga, ndi Leviyatani njoka yopindikapindika; nadzapha ching'ona chimene chili m'nyanja.


Ndipo mchenga wong'azimira udzasanduka thamanda, ndi nthaka yopanda madzi idzasanduka zitsime zamadzi; m'malo a ankhandwe m'mene iwo anagona, mudzakhala udzu ndi mabango ndi milulu.


Ndipo udzati kwa iwo mau awa, Maso anga agwe misozi usana ndi usiku, asaleke; pakuti namwali mwana wa anthu anga wasweka ndi kusweka kwakukulu, ndi bala lopweteka kwambiri.


nena, uziti, Atero Ambuye Yehova, Taona nditsutsana nawe, Farao mfumu ya Aejipito, ng'ona yaikulu yakugona m'kati mwa mitsinje yake, imene ikuti, Mtsinje wanga ndi wangatu, ndadzipangira ndekha uwu.


anthu akukhala mumdima adaona kuwala kwakukulu, ndi kwa iwo okhala m'malo a mthunzi wa imfa, kuwala kunatulukira iwo.


Ndipo chinaponyedwa pansi chinjoka chachikulu, njoka yokalambayo, iye wotchedwa mdierekezi ndi Satana, wonyenga wa dziko lonse; chinaponyedwa pansi kudziko, ndi angelo ake anaponyedwa naye pamodzi.


Ndipo chilombo ndinachionacho chinafanana ndi nyalugwe, ndi mapazi ake ngati mapazi a chimbalangondo, ndi pakamwa pake ngati pakamwa pa mkango; ndipo chinjoka chinampatsa iye mphamvu yake, ndi mpando wachifumu wake, ndi ulamuliro waukulu.


Ndipo wachisanu anatsanulira mbale yake pa mpando wachifumu wa chilombo; ndipo ufumu wake unadetsedwa; ndipo anatafuna malilime ao ndi kuwawa kwake,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa