Masalimo 44:19 - Buku Lopatulika19 mungakhale munatithyola mokhala zilombo, ndi kutiphimba nao mthunzi wa imfa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 mungakhale munatithyola mokhala zilombo, ndi kutiphimba nao mthunzi wa imfa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Komabe Inuyo mwatitswanya ndi kutisiya pakati pa nkhandwe ku chipululu, kumene kuli mdima wandiweyani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Koma Inu mwatiphwanya ndi kuchititsa kuti tikhale ozunzidwa ndi ankhandwe ndipo mwatiphimba ndi mdima waukulu. Onani mutuwo |