Masalimo 44:16 - Buku Lopatulika16 Chifukwa cha mau a wotonza wochitira mwano; chifukwa cha mdani ndi wobwezera chilango. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chifukwa cha mau a wotonza wochitira mwano; chifukwa cha mdani ndi wobwezera chilango. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 pakumva mau a anthu onditonza ndi onditukwana, poona mdani wanga ndi munthu wolipsira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 chifukwa cha mawu otonza a iwo amene amandinyoza ndi kundichita chipongwe, chifukwa cha mdani amene watsimikiza kubwezera. Onani mutuwo |