Masalimo 44:15 - Buku Lopatulika15 Tsiku lonse chimpepulo changa chikhala pamaso panga, ndipo manyazi a pankhope panga andikuta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Tsiku lonse chimpepulo changa chikhala pamaso panga, ndipo manyazi a pankhope panga andikuta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsiku lonse ndimangodziwona kuti ndine munthu wopandapake. Nkhope yanga yagwa chifukwa cha manyazi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Manyazi anga ali pamaso panga tsiku lonse ndipo nkhope yanga yaphimbidwa ndi manyazi Onani mutuwo |