Masalimo 44:14 - Buku Lopatulika14 Mutiika tikhale onyozeka mwa amitundu, ndi kuti anthu atipukusire mitu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Mutiika tikhale onyozeka mwa amitundu, ndi kuti anthu atipukusire mitu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Inu mwatisandutsa anthu oŵanyodola pakati pa anthu a mitundu ina, anthu omangosekedwa pakati pa anzathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Mwachititsa kuti tikhale onyozeka pakati pa anthu a mitundu ina; anthu amapukusa mitu yawo akationa. Onani mutuwo |