Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 44:13 - Buku Lopatulika

13 Mutisandutsa chotonza kwa anzathu, ndi choseketsa ndi cholalatitsa iwo akutizinga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Mutisandutsa chotonza kwa anzathu, ndi choseketsa ndi cholalatitsa iwo akutizinga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Inu mwatisandutsa anthu onyozeka kwa anzathu oyandikana nafe, anthu otizungulira amatiseka ndi kutinyodola.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Mwachititsa kuti tikhale chochititsa manyazi kwa anthu a mitundu ina, chonyozeka ndi chothetsa nzeru kwa iwo amene atizungulira.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 44:13
10 Mawu Ofanana  

Takhala chotonza cha anansi athu, ndi choseketsa ndi cholalatitsa iwo akutizinga.


Mutiika kuti atilimbirane anzathu; ndipo adani athu atiseka mwa iwo okha.


Onse opita panjirapa amfunkhira, akhala chotonza cha anansi ake.


Chimene adani anu, Yehova, atonza nacho; chimene atonzera nacho mayendedwe a wodzozedwa wanu.


Pakuti atero Yehova, Inu munagulitsidwa chabe, ndipo mudzaomboledwa opanda ndalama.


Ndipo ndidzawapatsa akhale choopsetsa choipa ku maufumu a dziko lapansi; akhale chitonzo ndi nkhani ndi choseketsa, ndi chitemberero, monse m'mene ndidzawapirikitsiramo.


Kodi sunaseke Israele? Kodi iye anapezedwa mwa mbala? Pakuti nthawi zonse unena za iye, upukusa mutu.


Ndipo mudzakhala chodabwitsa, ndi nkhani, ndi mwambi, mwa mitundu yonse ya anthu amene Yehova akutsogoleraniko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa