Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 40:15 - Buku Lopatulika

15 Apululuke, mobwezera manyazi ao amene anena nane, Hede, hede.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Apululuke, mobwezera manyazi ao amene anena nane, Hede, hede.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Amene amandinyodola kuti, “Ha, Ha,” achoke ndi kuchita manyazi poona kuti alephera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Iwo amene amanena kwa ine kuti, “Hee! Hee!” abwerere akuchita manyazi.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 40:15
10 Mawu Ofanana  

Achite manyazi nabwerere m'mbuyo. Onse akudana naye Ziyoni.


Ndipo andiyasamira m'kamwa mwao; nati, Hede, Hede, diso lathu lidachipenya.


Asanene mumtima mwao, Hede, momwemo! Asanene, Tammeza iye.


Achite manyazi, nadodome iwo akukondwera chifukwa cha choipa chidandigwera. Avekeke ndi manyazi ndi kupunzika iwo akudzikuza pa ine.


Ha? M'kamphindi ayesedwa bwinja; athedwa konse ndi zoopsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa