Masalimo 37:25 - Buku Lopatulika25 Ndinali mwana ndipo ndakalamba; ndipo sindinapenye wolungama atasiyidwa, kapena mbumba zake zilinkupempha chakudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndinali mwana ndipo ndakalamba; ndipo sindinapenya wolungama wasiyidwa, kapena mbumba zake zilinkupempha chakudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Chiyambire unyamata wanga mpaka ukalamba wanga uno, sindidaonepo munthu wabwino atasiyidwa ndi Mulungu, kapena ana ake akupempha chakudya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Ine ndinali wamngʼono ndipo tsopano ndakalamba koma sindinaonepo olungama akusiyidwa kapena ana awo akupempha chakudya. Onani mutuwo |