Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 37:22 - Buku Lopatulika

22 Pakuti iwo amene awadalitsa adzalandira dziko lapansi; koma iwo amene awatemberera adzadulidwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Pakuti iwo amene awadalitsa adzalandira dziko lapansi; koma iwo amene awatemberera adzadulidwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Anthu amene Chauta adaŵadalitsa, adzalandira dziko kuti likhale lao, koma amene Chauta adaŵatemberera adzaonongeka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Iwo amene Yehova amawadalitsa adzalandira dziko, koma amene Iye amawatemberera adzachotsedwa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 37:22
18 Mawu Ofanana  

Ndinapenya wopusa woyala mizu; koma pomwepo ndinatemberera pokhala pake.


Odalitsika inu a kwa Yehova, wakulenga kumwamba ndi dziko lapansi.


Munadzudzula odzikuza otembereredwa, iwo akusokera kusiyana nao malamulo anu.


Wodala yense wakuopa Yehova, wakuyenda m'njira zake.


Moyo wake udzakhala mokoma; ndi mbumba zake zidzalandira dziko lapansi.


Wodala munthuyo wokhululukidwa tchimo lake; wokwiriridwa choipa chake.


Koma ofatsa adzalandira dziko lapansi; nadzakondwera nao mtendere wochuluka.


Yehova adziwa masiku a anthu angwiro; ndipo cholowa chao chidzakhala chosatha.


Pakuti Yehova akonda chiweruzo, ndipo sataya okondedwa ake. Asungika kosatha, koma adzadula mbumba za oipa.


Pakuti ochita zoipa adzadulidwa; koma iwo akuyembekeza Yehova, iwowa adzalandira dziko lapansi.


Yehova atemberera za m'nyumba ya woipa; koma adalitsa mokhalamo olungama.


Pamene pakufuula iwe akupulumutse amene unawasonkhanitsa; koma mphepo idzawatenga, mpweya udzachotsa onse; koma iye amene andikhulupirira Ine adzakhala ndi dziko, nadzakhala nacho cholowa m'phiri langa lopatulika.


Pomwepo Iye adzanena kwa iwo a kudzanja lamanzere, Chokani kwa Ine otembereredwa inu, kumoto wa nthawi zonse wokolezedwera mdierekezi ndi angelo ake:


Ngati wina sakonda Ambuye, akhale wotembereredwa. Akudza Ambuye.


Pakuti onse amene atama ntchito za lamulo liwakhalira temberero; pakuti kwalembedwa, Wotembereredwa aliyense wosakhala m'zonse zolembedwa m'buku la chilamulo, kuzichita izi.


Khristu anatiombola ku temberero la chilamulo, atakhala temberero m'malo mwathu; pakuti kwalembedwa, Wotembereredwa aliyense wopachikidwa pamtengo.


Muziyenda m'njira yonse imene Yehova Mulungu wanu anakulamulirani, kuti mukakhale ndi moyo, ndi kuti chikukomereni, ndi kuti masiku anu achuluke m'dziko limene mudzakhala nalo lanulanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa