Masalimo 37:21 - Buku Lopatulika21 Woipa akongola, wosabweza, koma wolungama achitira chifundo, napereka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Woipa akongola, wosabweza, koma wolungama achitira chifundo, napereka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Munthu woipa amakonda ngongole koma satha kubweza, koma munthu wabwino ali ndi mtima wokoma ndi wopatsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Oyipa amabwereka ndipo sabweza koma olungama amapereka mowolowamanja. Onani mutuwo |