Masalimo 37:19 - Buku Lopatulika19 Sadzachita manyazi m'nyengo yoipa, ndipo m'masiku a njala adzakhuta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Sadzachita manyazi m'nyengo yoipa, ndipo m'masiku a njala adzakhuta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Pa nthaŵi ya mavuto sadzazunzika, pa nthaŵi yanjala, adzakhala nazo zakudya zochuluka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Pa nthawi ya mavuto iwo sadzafota; mʼmasiku a njala adzakhala ndi zinthu zambiri. Onani mutuwo |