Masalimo 37:18 - Buku Lopatulika18 Yehova adziwa masiku a anthu angwiro; ndipo cholowa chao chidzakhala chosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Yehova adziwa masiku a anthu angwiro; ndipo chosiyira chao chidzakhala chosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Chauta amasamalira moyo wa anthu angwiro, ndipo choloŵa chao chidzakhalapo mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Masiku a anthu osalakwa amadziwika ndi Yehova, ndipo cholowa chawo chidzakhala mpaka muyaya. Onani mutuwo |