Masalimo 37:16 - Buku Lopatulika16 Zochepa zake za wolungama zikoma koposa kuchuluka kwao kwa oipa ambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Zochepa zake za wolungama zikoma koposa kuchuluka kwao kwa oipa ambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Nkwabwino kukhala m'chilungamo ndi kusauka, kupambana kukhala nazo zokoma zambiri zimene munthu woipa ali nazo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Zabwino zochepa zimene olungama ali nazo ziposa chuma cha anthu oyipa ambiri; Onani mutuwo |