Masalimo 35:4 - Buku Lopatulika4 Athe nzeru nachite manyazi iwo akufuna moyo wanga; abwezedwe m'mbuyo nasokonezeke iwo akundipangira chiwembu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Athe nzeru nachite manyazi iwo akufuna moyo wanga; abwezedwe m'mbuyo nasokonezeke iwo akundipangira chiwembu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Anyozeke ndi kuchita manyazi onse ofunafuna moyo wanga. Abwezeni m'mbuyo ndipo athaŵe chinambalala amene apangana kuti andichite choipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iwo amene akufunafuna moyo wanga anyozedwe ndi kuchita manyazi; iwo amene akukonza kuti moyo wanga uwonongeke abwerere mʼmbuyo mochititsa mantha. Onani mutuwo |