Masalimo 35:3 - Buku Lopatulika3 Sololani nthungo, ndipo muwatsekerezere kunjira akundilondola. Nenani ndi moyo wanga, Chipulumutso chako ndine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Sololani nthungo, ndipo muwatsekerezere kunjira akundilondola. Nenani ndi moyo wanga, Chipulumutso chako ndine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tengani mkondo ndi nthungo, kuti mulimbane nawo anthu ondilondola. Uzani mtima wanga kuti, “Mpulumutsi wako ndine.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tengani mkondo ndi nthungo, kulimbana ndi iwo amene akundithamangitsa. Uzani moyo wanga kuti, “Ine ndine chipulumutso chako.” Onani mutuwo |